Yoswa 3:3 - Buku Lopatulika3 nalamulira anthu, ndi kuti, Mukadzaona likasa la chipangano la Yehova Mulungu wanu, ndi ansembe Aleviwo atalisenza, pamenepo muchoke kwanu ndi kulitsata. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 nalamulira anthu, ndi kuti, Mukadzaona likasa la chipangano la Yehova Mulungu wanu, ndi ansembe Aleviwo atalisenza, pamenepo muchoke kwanu ndi kulitsata. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 namauza anthu kuti, “Mukadzaona ansembe Achilevi aja atanyamula Bokosi lachipangano la Chauta, Mulungu wanu, mudzanyamuke pamalo panu ndi kuŵatsata. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 kulangiza anthu kuti, “Mukaona ansembe a Chilevi atanyamula Bokosi la Chipangano la Yehova Mulungu wanu, inu munyamuke pa malo ano ndi kumalitsatira. Onani mutuwo |