Yoswa 2:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo wina anaiuza mfumu ya Yeriko, kuti, Taonani, usiku uno alowa muno amuna a ana a Israele, kulizonda dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo wina anaiuza mfumu ya Yeriko, kuti, Taonani, usiku uno alowa muno amuna a ana a Israele, kulizonda dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mfumu ya mzinda wa Yerikowo idamva kuti, “Aisraele ena afika mumzinda muno usiku, kudzazonda dziko.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mfumu ya Yeriko inawuzidwa kuti, “Aisraeli ena afika mu mzinda muno usiku uno kudzazonda dziko.” Onani mutuwo |