Yoswa 13:3 - Buku Lopatulika3 kuyambira Sihori wokhala chakuno cha Ejipito mpaka malire a Ekeroni kumpoto, loyesedwa la Akanani; akalonga asanu a Afilisti, a ku Gaza, ndi a ku Asidodi, a ku Asikeloni, a ku Gati, ndi a ku Ekiro, ndi Avimu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 kuyambira Sihori wokhala chakuno cha Ejipito mpaka malire a Ekeroni kumpoto, loyesedwa la Akanani; akalonga asanu a Afilisti, a ku Gaza, ndi a ku Asidodi, a ku Asikeloni, a ku Gati, ndi a ku Ekiro, ndi Avimu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 (dziko limene layambira ku mtsinje wa Sihori kuvuma kwa Ejipito mpaka ku malire a Ekeroni, lonselo lili m'manja mwa Akanani. Olamulira dziko la Afilisti akukhala ku Gaza, ku Asidodi, ku Asikeloni, ku Gati ndi ku Ekeroni), ndiponso dziko la Avimu chakumwera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 kuchokera ku mtsinje wa Sihori kummawa kwa Igupto mpaka kumpoto kwa dziko la Ekroni. Madera onse amawerengedwa kuti ndi a Akanaani ngakhale amalamulidwa ndi mafumu asanu a Afilisti a ku Gaza, Asidodi, Asikeloni, Gati, Ekroni ndi Agiti, komanso ku Avimu ku chigawo cha kumpoto. Onani mutuwo |