Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 13:4 - Buku Lopatulika

4 kumwera dziko lonse la Akanani, ndi Meara ndiwo wa Asidoni, mpaka ku Afeki, mpaka ku malire a Aamori;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 kumwera dziko lonse la Akanani, ndi Meara ndiwo wa Asidoni, mpaka ku Afeki, mpaka ku malire a Aamori;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Palinso dziko la Akanani ndi la Meala, lomwe lili m'manja mwa Asidoni mpaka ku Afeki, malo amene ali pafupi ndi malire a Aamori.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Dziko lina la Akanaani ndi Ameara limene lili mʼmanja mwa Asidoni mpaka ku Afeki, dziko limene linachitana malire ndi dziko la Aamori.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 13:4
11 Mawu Ofanana  

Tsono kunachitika, pakufikanso chaka Benihadadi anamemeza Aaramu nakwera ku Afeki kukaponyana ndi Aisraele.


Ndipo otsalawo anathawira ku Afeki kumzinda, ndipo linga linawagwera anthu zikwi makumi awiri mphambu asanu ndi awiri amene adatsalawo. Ndipo Benihadadi anathawa, nalowa m'mzinda, m'chipinda cha m'katimo.


Atero Ambuye Yehova kwa Yerusalemu, Chiyambi chako ndi kubadwa kwako ndiko kudziko la Akanani; atate wako anali Mwamori, ndi mai wako Muhiti.


Ndipo ndinakukwezani kuchokera m'dziko la Ejipito, ndi kukutsogolerani zaka makumi anai m'chipululu, kuti mulandire dziko la Aamori likhale cholowa chanu.


Motero Yoswa anakantha dziko lonse, la kumapiri, la kumwera, la kuchidikha, la kuzigwa, ndi mafumu ao onse; sanasiyepo ndi mmodzi yense; koma anaononga psiti zonse zampweya, monga Yehova Mulungu wa Israele adalamulira.


kwa Akanani kum'mawa ndi kumadzulo, ndi kwa Aamori ndi Ahiti, ndi Aperizi ndi Ayebusi kumapiri, ndi kwa Ahivi kunsi kwa Heremoni, m'dziko la Mizipa.


mfumu ya ku Afeki, imodzi; mfumu ya ku Lasaroni, imodzi;


Uma womwe ndi Afeki, ndi Rehobu; mizinda makumi awiri mphambu iwiri ndi midzi yao.


Ndipo mau a Samuele anafikira kwa Aisraele onse. Ndipo Aisraele anatuluka kukaponyana nkhondo ndi Afilisti, namanga zithando zao ku Ebenezeri; Afilistiwo namanga mu Afeki.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa