Yoswa 13:4 - Buku Lopatulika4 kumwera dziko lonse la Akanani, ndi Meara ndiwo wa Asidoni, mpaka ku Afeki, mpaka ku malire a Aamori; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 kumwera dziko lonse la Akanani, ndi Meara ndiwo wa Asidoni, mpaka ku Afeki, mpaka ku malire a Aamori; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Palinso dziko la Akanani ndi la Meala, lomwe lili m'manja mwa Asidoni mpaka ku Afeki, malo amene ali pafupi ndi malire a Aamori. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Dziko lina la Akanaani ndi Ameara limene lili mʼmanja mwa Asidoni mpaka ku Afeki, dziko limene linachitana malire ndi dziko la Aamori. Onani mutuwo |