Yoswa 11:3 - Buku Lopatulika3 kwa Akanani kum'mawa ndi kumadzulo, ndi kwa Aamori ndi Ahiti, ndi Aperizi ndi Ayebusi kumapiri, ndi kwa Ahivi kunsi kwa Heremoni, m'dziko la Mizipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 kwa Akanani kum'mawa ndi kumadzulo, ndi kwa Aamori ndi Ahiti, ndi Aperizi ndi Ayebusi kumapiri, ndi kwa Ahivi kunsi kwa Heremoni, m'dziko la Mizipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Adatumizanso uthenga kwa Akanani a pa mbali zonse ziŵiri za Yordani, kwa Aamori, Ahiti, Aperizi ndi Ayebusi a ku dziko lamapiri, mpakanso kwa Ahivi amene ankakhala patsinde pa phiri la Heremoni m'dziko la Mizipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Inatumizanso uthenga kwa Akanaani amene ankakhala kummawa ndi kumadzulo kwa Yorodani. Uthenga unapitanso kwa Aamori, Ahiti, Aperezi ndi Ayebusi amene amakhala mʼdziko la ku mapiri ndiponso kwa Ahivi amene ankakhala mʼmunsi mwa phiri la Herimoni ku chigwa cha Mizipa. Onani mutuwo |