Yoswa 11:2 - Buku Lopatulika2 ndi kwa mafumu akukhala kumpoto kumapiri, ndi kuchigwa kumwera kwa Kineroti, ndi kuchidikha, ndi ku mitunda ya Dori kumadzulo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 ndi kwa mafumu akukhala kumpoto kumapiri, ndi kuchigwa kumwera kwa Kineroti, ndi kuchidikha, ndi ku mitunda ya Dori kumadzulo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adatumizanso uthenga kwa mafumu a ku dziko lamapiri kumpoto kwa chigwa cha Yordani, kumwera kwa nyanja ya Galilea, m'dziko la chigwa cha Yordani ndiponso kumbali kwa nyanja, kufupi ndi Dori. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Inatumizanso uthenga kwa mafumu a kumpoto, kumapiri, ndi mʼchigwa cha Yorodani kummwera kwa nyanja ya Kinereti, ndiponso kumadzulo mʼmbali mwa nyanja pafupi ndi Dori. Onani mutuwo |