Yoswa 11:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo anatuluka, iwo ndi makamu ao onse nao, anthu ambiri, kuchuluka kwao ngati mchenga uli m'mphepete mwa nyanja; ndi akavalo ndi magaleta ambirimbiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo anatuluka, iwo ndi makamu ao onse nao, anthu ambiri, kuchuluka kwao ngati mchenga uli m'mphepete mwa nyanja; ndi akavalo ndi magaleta ambirimbiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mafumuwo adabwera ndi ankhondo ao onse, ndipo kuchuluka kwao kwa ankhondowo kunali ngati mchenga wa m'mbali mwa nyanja. Anali ndi akavalo ambiri, pamodzi ndi magaleta omwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mafumuwo anabwera pamodzi ndi ankhondo awo onse. Gulu la ankhondo linali lalikulu ngati mchenga wa mʼmbali mwa nyanja. Analinso ndi akavalo ndi magaleta ambiri. Onani mutuwo |