Yona 3:2 - Buku Lopatulika2 Nyamuka, pita ku Ninive mzinda waukulu uja, nuulalikire uthenga umene ndikuuza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nyamuka, pita ku Ninive mudzi waukulu uja, nuulalikire uthenga umene ndikuuza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Nyamuka, pita ku Ninive, mzinda waukulu uja, ukaulalikire uthenga umene ndikukuuza.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Nyamuka, pita ku mzinda waukulu wa Ninive ndipo ukalalikire uthenga umene ndikupatsa.” Onani mutuwo |