Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yona 3:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yona nthawi yachiwiri, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yona nthawi yachiwiri, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Chauta adalankhula ndi Yona kachiŵiri, namuuza kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ndipo Yehova anayankhula ndi Yona kachiwiri kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yona 3:1
6 Mawu Ofanana  

Aneneri amene analipo kale ndisanakhale ine, nimusanakhale inu, ananenera maiko ambiri, ndi mafumu aakulu, za nkhondo, ndi za choipa, ndi za mliri.


Mkango ukabangula, ndani amene saopa? Ambuye Yehova wanena, ndani amene sanenera?


Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yona mwana wa Amitai, ndi kuti,


Pamenepo Yehova analankhula ndi nsombayo, ndipo inamsanzira Yona kumtunda.


Nyamuka, pita ku Ninive mzinda waukulu uja, nuulalikire uthenga umene ndikuuza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa