Yohane 9:40 - Buku Lopatulika40 Ndipo Afarisi ena akukhala ndi Iye anamva izi, nati kwa Iye, Kodi ifenso ndife osaona? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Ndipo Afarisi ena akukhala ndi Iye anamva izi, nati kwa Iye, Kodi ifenso ndife osaona? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Afarisi ena amene anali pafupi naye, atamva zimenezi adamufunsa kuti, “Kodi monga ifenso ndife akhungu?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Afarisi ena amene anali pafupi naye anamva akunena izi ndipo anafunsa kuti, “Chiyani? Kodi ndife osaonanso?” Onani mutuwo |