Yohane 9:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo Yesu anati, Kudzaweruza ndadza Ine kudziko lino lapansi, kuti iwo osapenya apenye; ndi kuti iwo akupenya akhale osaona. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo Yesu anati, Kudzaweruza ndadza Ine kudziko lino lapansi, kuti iwo osapenya apenye; ndi kuti iwo akupenya akhale osaona. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Tsono Yesu adati, “Ndidabwera pansi pano kudzaweruza, kuti osapenya apenye, ndipo openya achite khungu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Yesu anati, “Ndinabwera pansi pano kudzaweruza kuti osaona aone ndi openya asaone.” Onani mutuwo |