Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 9:38 - Buku Lopatulika

38 Koma iye anati, Ndikhulupirira, Ambuye; ndipo anamgwadira Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Koma iye anati, Ndikhulupirira, Ambuye; ndipo anamgwadira Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Iye adati, “Ambuye, ndikukhulupirira.” Atatero adamgwadira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Pamenepo munthuyo anati, “Ambuye, ndikukhulupirira,” ndipo anamulambira Iye.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 9:38
10 Mawu Ofanana  

Mpsompsoneni Mwanayo, kuti angakwiye, ndipo mungatayike m'njira ukayaka pang'ono pokha mkwiyo wake. Odala onse akumkhulupirira Iye.


potero mfumuyo adzakhumba kukoma kwako, pakuti ndiye mbuye wako; ndipo iwe umgwadire iye.


Ndipo iwo amene anali m'ngalawamo anamgwadira, nanena, Zoonadi, ndinu Mwana wa Mulungu.


Ndipo pamene anamuona Iye, anamlambira; koma ena anakayika.


Ndipo onani, Yesu anakomana nao, nanena, Tikuoneni. Ndipo iwo anadza, namgwira Iye mapazi ake, namgwadira.


Ndipo onani, wakhate anadza namgwadira Iye, nanena, Ambuye ngati mufuna mungathe kundikonza.


Ndipo anamlambira Iye, nabwera ku Yerusalemu ndi chimwemwe chachikulu;


Tomasi anayankha nati kwa Iye, Ambuye wanga, ndi Mulungu wanga.


Ndipo Yesu anati, Kudzaweruza ndadza Ine kudziko lino lapansi, kuti iwo osapenya apenye; ndi kuti iwo akupenya akhale osaona.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa