Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 9:36 - Buku Lopatulika

36 Iyeyu anayankha nati, Ndipo ndani Iye, Ambuye, kuti ndimkhulupirire Iye?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Iyeyu anayankha nati, Ndipo ndani Iye, Ambuye, kuti ndimkhulupirire Iye?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Iye adati, “Ambuye, mundiwuzetu ndani Iyeyo, kuti ndimkhulupirire.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Munthuyo anafunsa kuti, “Kodi, Ambuye, ameneyo ndi ndani? Ndiwuzeni kuti ndimukhulupirire Iye?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 9:36
6 Mawu Ofanana  

Bwenzi lako aposa abwenzi ena bwanji, mkaziwe woposa kukongola? Bwenzi lako aposa abwenzi ena bwanji, kuti utilumbirira motero?


nati kwa Iye, Inu ndinu wakudza kodi, kapena tiyembekezere wina?


Koma Yesu anacheuka, napenya iwo alikumtsata, nanena nao, Mufuna chiyani? Ndipo anati kwa Iye, Rabi (ndiko kunena posandulika, Mphunzitsi), mukhala kuti?


Yesu anati kwa iye, Wamuona Iye, ndiponso wakulankhula ndi iwe ndi Iyeyo.


Ndipo iwo adzaitana bwanji pa Iye amene sanamkhulupirire? Ndipo adzakhulupirira bwanji Iye amene sanamve za Iye? Ndipo adzamva bwanji wopanda wolalikira?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa