Yohane 9:35 - Buku Lopatulika35 Yesu anamva kuti adamtaya kunja; ndipo pakumpeza iye, anati, Kodi ukhulupirira Mwana wa Munthu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Yesu anamva kuti adamtaya kunja; ndipo pakumpeza iye, anati, Kodi ukhulupirira Mwana wa Munthu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Yesu adamva kuti Ayuda amtulutsa ndi kumdula ku mpingo munthu uja. Tsono pamene adampeza, adamufunsa kuti, “Kodi ukukhulupirira Mwana wa Munthu?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Yesu anamva kuti anamutulutsa kunja ndipo pamene anamupeza anati, “Kodi ukukhulupirira Mwana wa Munthu?” Onani mutuwo |