Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 9:37 - Buku Lopatulika

37 Yesu anati kwa iye, Wamuona Iye, ndiponso wakulankhula ndi iwe ndi Iyeyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Yesu anati kwa iye, Wamuona Iye, ndiponso wakulankhula ndi iwe ndi Iyeyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Yesu adamuuza kuti, “Wamuwona kale, ndi yemwe akulankhula nawe.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Yesu anati, “Iwe wamuona tsopano. Zoonadi ndiye amene akuyankhula nawe.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 9:37
10 Mawu Ofanana  

Chinsinsi cha Yehova chili kwa iwo akumuopa Iye; ndipo adzawadziwitsa pangano lake.


Iwe waona zinthu zambiri, koma susamalira konse; makutu ako ali otseguka, koma sumva konse.


Nyengo imeneyo Yesu anayankha nati, Ndivomerezana ndi Inu, Atate, Ambuye wakumwamba ndi dziko lapansi, kuti munazibisira izo kwa anzeru ndi akudziwitsa, ndipo munaziululira zomwe kwa makanda:


Yesu ananena naye, Ine wakulankhula nawe ndine amene.


Ngati munthu aliyense afuna kuchita chifuniro chake, adzazindikira za chiphunzitsocho, ngati chichokera kwa Mulungu, kapena ndilankhula zochokera kwa Ine ndekha.


Koma iye anati, Ndikhulupirira, Ambuye; ndipo anamgwadira Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa