Yohane 9:34 - Buku Lopatulika34 Anayankha nati kwa iye, Wabadwa iwe konse m'zoipa, ndipo iwe utiphunzitse ife kodi? Ndipo anamtaya kunja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Anayankha nati kwa iye, Wabadwa iwe konse m'zoipa, ndipo iwe utiphunzitse ife kodi? Ndipo anamtaya kunja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Iwo adati, “Iwe udabadwa m'machimo okhaokha. Ndiye iweyo nkutiphunzitsa ife?” Atatero adamtulutsa nkumudula ku mpingo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Pamenepo anayankha kuti, “Iwe unabadwa mu uchimo kotheratu; bwanji ukuyesa kutiphunzitsa ife!” Ndipo anamutulutsa kunja. Onani mutuwo |