Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 8:57 - Buku Lopatulika

57 Ayuda pamenepo anati kwa Iye, Simunafikire zaka makumi asanu, ndipo munaona Abrahamu kodi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

57 Ayuda pamenepo anati kwa Iye, Simunafikire zaka makumi asanu, ndipo munaona Abrahamu kodi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

57 Apo Ayuda adamufunsa kuti, “Zaka zako sizinakwane ndi makumi asanu omwe, ndiye nkukhala utaona Abrahamu?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

57 Ayuda anati kwa Iye, “Inu sumunafike nʼkomwe zaka makumi asanu, ndipo mukuti munamuona Abrahamu!”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 8:57
2 Mawu Ofanana  

Ndipo umene ndiwo umboni wa Yohane, pamene Ayuda anatuma kwa iye ansembe ndi Alevi a ku Yerusalemu akamfunse iye, Ndiwe yani?


Yesu anati kwa iwo, Indetu, indetu, ndinena kwa inu, asanayambe kukhala Abrahamu ndipo Ine ndilipo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa