Yohane 8:58 - Buku Lopatulika58 Yesu anati kwa iwo, Indetu, indetu, ndinena kwa inu, asanayambe kukhala Abrahamu ndipo Ine ndilipo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201458 Yesu anati kwa iwo, Indetu, indetu, ndinena kwa inu, asanayambe kukhala Abrahamu ndipo Ine ndilipo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa58 Yesu adati, “Ndithu ndikunenetsa kuti Abrahamu asanabadwe, Ine ndilipo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero58 Yesu anayankha kuti, “Ine ndikukuwuzani choonadi, Abrahamu asanabadwe, Ine Ndine!” Onani mutuwo |