Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 8:56 - Buku Lopatulika

56 Atate wanu Abrahamu anakondwera kuona tsiku langa; ndipo anaona nasangalala.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

56 Atate wanu Abrahamu anakondwera kuona tsiku langa; ndipo anaona nasangalala.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

56 Atate anu Abrahamu adaasekera poyembekeza kuti adzaona tsiku la kubwera kwanga. Adaliwonadi nakondwa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

56 Abambo anu Abrahamu anakondwera poyembekezera kubwera kwanga. Iwo anandiona ndipo anasangalala.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 8:56
11 Mawu Ofanana  

m'mbeu zako mitundu yonse ya dziko lapansi idzadalitsidwa: chifukwa wamvera mau anga.


Pakuti indetu ndinena kwa inu, kuti aneneri ambiri ndi anthu olungama analakalaka kupenya zimene muziona, koma sanazione; ndi kumva zimene muzimva, koma sanazimve.


Pakuti ndinena ndi inu kuti aneneri ndi mafumu ambiri anafuna kuona zimene inu muziona, koma sanazione; ndi kumva zimene mukumva, koma sanazimve.


Yesu anayankha iwo, Ndakuuzani, ndipo simukhulupirira. Ntchitozi ndidzichita Ine m'dzina la Atate wanga, zimenezi zindichitira umboni.


Ndidziwa kuti muli mbeu ya Abrahamu; koma mufuna kundipha Ine, chifukwa mau anga alibe malo mwa inu.


Anayankha nati kwa iye, Atate wathu ndiye Abrahamu. Yesu ananena nao, Ngati muli ana a Abrahamu, mukadachita ntchito za Abrahamu.


Iwo onse adamwalira m'chikhulupiriro, osalandira malonjezano, komatu adawaona ndi kuwalankhula kutali, navomereza kuti ali alendo ndi ogonera padziko.


Ndipo iwo onse adachitidwa umboni mwa chikhulupiriro, sanalandire lonjezanolo,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa