Yohane 8:48 - Buku Lopatulika48 Ayuda anayankha nati kwa Iye, Kodi sitinenetsa kuti Inu ndinu Msamariya, ndipo muli ndi chiwanda? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Ayuda anayankha nati kwa Iye, Kodi sitinenetsa kuti Inu ndinu Msamariya, ndipo muli ndi chiwanda? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Ayuda aja pomuyankha Yesu, adati, “Kodi ife sitikunena zoona kuti Iwe ndiwe Msamariya, ndipo kuti ndiwe wogwidwa ndi mizimu yoipa?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Ayuda anamuyankha Iye kuti, “Kodi ife sitikulondola ponena kuti Inu ndi Msamariya ndi wogwidwa ndi chiwanda?” Onani mutuwo |