Yohane 8:47 - Buku Lopatulika47 Iye wochokera kwa Mulungu amva zonena za Mulungu; inu simumva chifukwa chakuti simuli a kwa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Iye wochokera kwa Mulungu amva zonena za Mulungu; inu simumva chifukwa chakuti simuli a kwa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Munthu wochokera kwa Mulungu amatchera khutu ku mau a Mulungu. Koma inu simuchokera kwa Mulungu ai, nchifukwa chake simutchera khutu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Munthu wochokera kwa Mulungu amamva zimene Mulungu amanena. Chifukwa chimene simumvera nʼchakuti, inuyo sindinu ochokera kwa Mulungu.” Onani mutuwo |