Yohane 8:46 - Buku Lopatulika46 Ndani mwa inu anditsutsa Ine za tchimo? Ngati ndinena choonadi, simundikhulupirira Ine chifukwa ninji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Ndani mwa inu anditsutsa Ine za tchimo? Ngati ndinena choonadi, simundikhulupirira Ine chifukwa ninji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Kodi ndani mwa inu anganditsimikize kuti ndine wochimwa? Nanga ngati ndikunena zoona, mukulekeranji kundikhulupirira? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Ndani mwa inu angatsimikize kuti ndine wochimwa? Ngati Ine ndikunena choonadi, nʼchifukwa chiyani simukundikhulupirira? Onani mutuwo |