Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 8:36 - Buku Lopatulika

36 Chifukwa chake ngati Mwana adzakuyesani inu aufulu, mudzakhala mfulu ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Chifukwa chake ngati Mwana adzakuyesani inu aufulu, mudzakhala mfulu ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Tsono ngati Mwana akumasulani, mudzakhaladi mfulu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Nʼchifukwa chake ngati Mwana adzakumasulani, mudzakhala mfulu ndithu.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 8:36
12 Mawu Ofanana  

Khazikitsani mapazi anga m'mau anu; ndipo zisandigonjetse zopanda pake zilizonse.


Ndidzathamangira njira ya malamulo anu, mutakulitsa mtima wanga.


Ndiponso muletse kapolo wanu pa zodzitama; zisachite ufumu pa ine. Pamenepo ndidzakhala wangwiro, ndi wosachimwa cholakwa chachikulu.


Mzimu wa Ambuye Yehova uli pa ine; pakuti Yehova wandidzoza ine ndilalikire mau abwino kwa ofatsa; Iye wanditumiza ndikamange osweka mtima, ndikalalikire kwa am'nsinga mamasulidwe, ndi kwa omangidwa kutsegulidwa kwa m'ndende;


Mzimu wa Ambuye uli pa Ine, chifukwa chake Iye anandidzoza Ine ndiuze anthu osauka Uthenga Wabwino: anandituma Ine kulalikira am'nsinga mamasulidwe, ndi akhungu kuti apenyanso, kutulutsa ndi ufulu ophwanyika,


Pakuti chilamulo cha mzimu wa moyo mwa Khristu Yesu chandimasula ine ku lamulo la uchimo ndi la imfa.


Pakuti iye amene anaitanidwa mwa Ambuye, pokhala ali kapolo, ali mfulu ya Ambuye: momwemonso woitanidwayo, pokhala ali mfulu, ali kapolo wa Khristu.


Koma Ambuye ndiye Mzimuyo; ndipo pamene pali Mzimu wa Ambuye pali ufulu.


Khristu anatisandutsa mfulu, kuti tikhale mfulu; chifukwa chake chilimikani, musakodwenso ndi goli la ukapolo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa