Yohane 8:36 - Buku Lopatulika36 Chifukwa chake ngati Mwana adzakuyesani inu aufulu, mudzakhala mfulu ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Chifukwa chake ngati Mwana adzakuyesani inu aufulu, mudzakhala mfulu ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Tsono ngati Mwana akumasulani, mudzakhaladi mfulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Nʼchifukwa chake ngati Mwana adzakumasulani, mudzakhala mfulu ndithu. Onani mutuwo |