Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 8:35 - Buku Lopatulika

35 Koma kapolo sakhala m'nyumba nthawi yonse; mwana ndiye akhala nthawi yonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Koma kapolo sakhala m'nyumba nthawi yonse; mwana ndiye akhala nthawi yonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Kapolo sakhala nao m'banja nthaŵi zonse, koma mwana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 8:35
13 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake anati kwa Abrahamu, Chotsa mdzakazi uyo, ndi mwana wake wamwamuna; chifukwa mwana wa mdzakazi uyo sadzalowa m'nyumba pamodzi naye mwana wanga Isaki.


Koma akapatsa mphatso yotenga kucholowa chake kwa wina wa anyamata ake, idzakhala yake mpaka chaka cha ufulu; pamenepo ibwerere kwa kalonga, koma cholowa chake chikhale cha ana ake.


Koma iye ananena naye, Mwana wanga, iwe uli ndine nthawi zonse, ndipo zanga zonse zili zako.


Pakuti munafa, ndipo moyo wanu wabisika pamodzi ndi Khristu mwa Mulungu.


koma Iye chifukwa kuti akhala Iye nthawi yosatha ali nao unsembe wosasinthika,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa