Yohane 8:35 - Buku Lopatulika35 Koma kapolo sakhala m'nyumba nthawi yonse; mwana ndiye akhala nthawi yonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Koma kapolo sakhala m'nyumba nthawi yonse; mwana ndiye akhala nthawi yonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Kapolo sakhala nao m'banja nthaŵi zonse, koma mwana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse. Onani mutuwo |