Yohane 8:37 - Buku Lopatulika37 Ndidziwa kuti muli mbeu ya Abrahamu; koma mufuna kundipha Ine, chifukwa mau anga alibe malo mwa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndidziwa kuti muli mbeu ya Abrahamu; koma mufuna kundipha Ine, chifukwa mau anga alibe malo mwa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Ndikudziŵa kuti ndinu ana a Abrahamu, komabe mukufuna kundipha, chifukwa simukuvomereza mau anga m'mitima mwanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Ine ndikudziwa kuti inu ndinu zidzukulu za Abrahamu. Chonsecho inu mwakonzeka kundipha Ine, chifukwa mawu anga alibe malo mwa inu. Onani mutuwo |