Yohane 8:34 - Buku Lopatulika34 Yesu anayankha iwo, nati, Indetu, indetu, ndinena kwa inu kuti yense wakuchita tchimo ali kapolo wa tchimolo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Yesu anayankha iwo, nati, Indetu, indetu, ndinena kwa inu kuti yense wakuchita tchimo ali kapolo wa chimolo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Yesu adaŵayankha kuti, “Ndithu ndikunenetsa kuti aliyense wochita tchimo ndi kapolo wa tchimolo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Yesu anayankha kuti, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wochita tchimo ndi kapolo wa tchimolo. Onani mutuwo |