Yohane 8:27 - Buku Lopatulika27 Sanazindikira iwo kuti analikunena nao za Atate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Sanazindikira iwo kuti analikunena nao za Atate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Anthu aja sadazindikire kuti Yesu akunena za Atate. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Iwo sanazindikire kuti Iye amawawuza za Atate ake. Onani mutuwo |