Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 8:27 - Buku Lopatulika

27 Sanazindikira iwo kuti analikunena nao za Atate.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Sanazindikira iwo kuti analikunena nao za Atate.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Anthu aja sadazindikire kuti Yesu akunena za Atate.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Iwo sanazindikire kuti Iye amawawuza za Atate ake.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 8:27
9 Mawu Ofanana  

Tiyambasira khoma ngati wakhungu, inde tiyambasa monga iwo opanda maso; tiphunthwa usana monga m'chizirezire; tili m'malo amdima ngati akufa.


Ndipo Iye anati, Kauze anthu awa, Imvani inu ndithu, koma osazindikira; yang'anani inu ndithu, koma osadziwitsa.


Ndili nazo zambiri zakulankhula ndi zakuweruza za inu; koma wondituma Ine ali woona; ndipo zimene ndazimva kwa Iye, zomwezo ndilankhula kwa dziko lapansi.


Chifukwa chake Yesu anati, Pamene mutadzamkweza Mwana wa Munthu, pomwepo mudzazindikira kuti Ine ndine, ndipo sindichita kanthu kwa Ine ndekha, koma monga anandiphunzitsa Atate, ndilankhula izi.


Simuzindikira malankhulidwe anga chifukwa ninji? Chifukwa simungathe kumva mau anga.


Iye wochokera kwa Mulungu amva zonena za Mulungu; inu simumva chifukwa chakuti simuli a kwa Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa