Yohane 8:25 - Buku Lopatulika25 Pamenepo ananena kwa Iye, Ndinu yani? Yesu anati kwa iwo, Chimene chomwe ndidalankhulanso ndi inu kuyambira pachiyambi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Pamenepo ananena kwa Iye, Ndinu yani? Yesu anati kwa iwo, Chimene chomwe ndidalankhulanso ndi inu kuyambira pachiyambi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Apo iwo adamufunsa kuti, “Iweyo ndiwe yani?” Yesu adati, “Nchomwe ndakhala ndikukuuzani chiyambire ndithu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Iwo anafunsa kuti, “Ndinu ndani?” Yesu anayankha kuti, “Monga Ine ndakhala ndikunena nthawi yonseyi, Onani mutuwo |