Yohane 8:20 - Buku Lopatulika20 Mau awa analankhula m'nyumba yosungiramo chuma cha Mulungu pophunzitsa mu Kachisi; ndipo palibe munthu anamgwira Iye, pakuti nthawi yake siinafike. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Mau awa analankhula m'nyumba yosungiramo chuma cha Mulungu pophunzitsa m'Kachisi; ndipo palibe munthu anamgwira Iye, pakuti nthawi yake siinafike. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Yesu adanena mau ameneŵa pamene ankaphunzitsa m'Nyumba ya Mulungu, m'chipinda cholandiriramo zopereka za anthu. Panalibe amene adamgwira, chifukwa nthaŵi yake inali isanafike. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Iye anayankhula mawu awa pamene amaphunzitsa Nyumba ya Mulungu pafupi ndi malo amene amaponyapo zopereka. Komabe palibe amene anamugwira Iye, chifukwa nthawi yake inali isanakwane. Onani mutuwo |