Yohane 8:19 - Buku Lopatulika19 Chifukwa chake ananena ndi Iye, Ali kuti Atate wanu? Yesu anayankha, Simudziwa kapena Ine, kapena Atate wanga; mukadadziwa Ine, mukadadziwanso Atate wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Chifukwa chake ananena ndi Iye, Ali kuti Atate wanu? Yesu anayankha, Simudziwa kapena Ine, kapena Atate wanga; mukadadziwa Ine, mukadadziwanso Atate wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Apo iwo adamufunsa kuti, “Atate akowo ali kuti?” Yesu adati, “Ine simundidziŵa, Atate anganso simuŵadziŵa. Mukadandidziŵa, bwenzi mutaŵadziŵanso Atate anga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Kenaka iwo anamufunsa Iye kuti, “Kodi Atate anuwo ali kuti?” Yesu anayankha kuti, “Inu simundidziwa Ine. Atate anganso simuwadziwa. Mukanandidziwa Ine, mukanawadziwanso Atate anga.” Onani mutuwo |