Yohane 8:18 - Buku Lopatulika18 Ine ndine wakuchita umboni wa Ine ndekha, ndipo Atate amene anandituma Ine achita umboni wa Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ine ndine wakuchita umboni wa Ine ndekha, ndipo Atate amene anandituma Ine achita umboni wa Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ine ndimadzichitira ndekha umboni, nawonso Atate amene adandituma amandichitira umboni.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ine ndikudzichitira ndekha umboni; ndipo mboni inanso ndi Atate amene anandituma.” Onani mutuwo |