Yohane 8:17 - Buku Lopatulika17 Inde kudalembedwa m'chilamulo chanu kuti umboni wa anthu awiri uli woona. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Inde kudalembedwa m'chilamulo chanu kuti umboni wa anthu awiri uli woona. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ndipo m'Malamulo anu mudalembedwa kuti umboni wa anthu aŵiri ngwokwanira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Mʼmalamulo anu munalembedwa kuti umboni wa anthu awiri ndi wovomerezeka. Onani mutuwo |