Yohane 7:49 - Buku Lopatulika49 Koma khamu ili losadziwa chilamulo, likhala lotembereredwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201449 Koma khamu ili losadziwa chilamulo, likhala lotembereredwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa49 Koma anthu wambaŵa sadziŵa Malamulo a Mose; ngotembereredwa basi!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero49 Ayi! Koma gulu limene silidziwa malamulo ndi lotembereredwa.” Onani mutuwo |