Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 7:48 - Buku Lopatulika

48 Kodi wina wa akulu anakhulupirira Iye, kapena wa Afarisi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

48 Kodi wina wa akulu anakhulupirira Iye, kapena wa Afarisi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

48 Kodi mudamvapo kuti pakati pa akuluakulu kapena pakati pa Afarisi alipo wokhulupirira amene uja?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

48 “Kodi alipo ena a olamulira kapena a Afarisi, anamukhulupirira Iye?

Onani mutuwo Koperani




Yohane 7:48
12 Mawu Ofanana  

Nyengo imeneyo Yesu anayankha nati, Ndivomerezana ndi Inu, Atate, Ambuye wakumwamba ndi dziko lapansi, kuti munazibisira izo kwa anzeru ndi akudziwitsa, ndipo munaziululira zomwe kwa makanda:


Ndipo Pilato anaitana ansembe aakulu, ndi akulu, ndi anthu, asonkhane,


Kungakhale kotero, ambiri a mwa akulu anakhulupirira Iye; koma chifukwa cha Afarisi sanavomereze, kuti angaletsedwe m'sunagoge,


Koma panali munthu wa Afarisi, dzina lake Nikodemo, mkulu wa Ayuda.


Ndipo taona amalankhula poyera, ndipo sanena kanthu kwa Iye. Kapena kodi akulu adziwa ndithu kuti ndiye Khristu ameneyo?


Koma khamu ili losadziwa chilamulo, likhala lotembereredwa.


Nikodemo ananena kwa iwo, amene uja adadza kwa Iye kale, ali mmodzi wa iwo,


Ndipo mau a Mulungu anakula; ndipo chiwerengero cha ophunzira chidachulukatu ku Yerusalemu; ndipo khamu lalikulu la ansembe linamvera chikhulupirirocho.


Ali kuti wanzeru? Mlembi ali kuti? Ali kuti wotsutsana wa nthawi ya pansi pano? Kodi Mulungu sanaipusitse nzeru ya dziko lapansi?


imene saidziwa mmodzi wa akulu a nthawi ya pansi pano: pakuti akadadziwa sakadapachika Mbuye wa ulemerero;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa