Yohane 7:48 - Buku Lopatulika48 Kodi wina wa akulu anakhulupirira Iye, kapena wa Afarisi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Kodi wina wa akulu anakhulupirira Iye, kapena wa Afarisi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Kodi mudamvapo kuti pakati pa akuluakulu kapena pakati pa Afarisi alipo wokhulupirira amene uja? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 “Kodi alipo ena a olamulira kapena a Afarisi, anamukhulupirira Iye? Onani mutuwo |