Yohane 7:47 - Buku Lopatulika47 Pamenepo Afarisi anayankha iwo, Kodi mwasokeretsedwa inunso? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Pamenepo Afarisi anayankha iwo, Kodi mwasokeretsedwa inunso? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Apo Afarisi adati, “Kani inunso wakunyengani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Afarisi anawadzudzula nati, “Kodi mukutanthauza kuti Iye anakunamizani inunso?” Onani mutuwo |