Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 7:46 - Buku Lopatulika

46 Anyamatawo anayankha, Nthawi yonse palibe munthu analankhula chotero.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

46 Anyamatawo anayankha, Nthawi yonse palibe munthu analankhula chotero.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

46 Asilikali aja adayankha kuti, “Palibenso wina amene adalankhulapo ngati munthu ameneyo nkale lonse.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

46 Asilikali aja anati, “Palibe wina amene anayankhula ngati Munthu ameneyo nʼkale lonse.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 7:46
5 Mawu Ofanana  

Ndipo onse anamchitira Iye umboni nazizwa ndi mau a chisomo akutuluka m'kamwa mwake; nanena, Kodi uyu si mwana wa Yosefe?


chifukwa mau ake anali ndi ulamuliro.


Ndipo taona amalankhula poyera, ndipo sanena kanthu kwa Iye. Kapena kodi akulu adziwa ndithu kuti ndiye Khristu ameneyo?


Afarisi anamva khamu la anthu ling'ung'udza zimenezi za Iye; ndipo ansembe aakulu ndi Afarisi anatuma anyamata kuti akamgwire Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa