Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 7:45 - Buku Lopatulika

45 Pamenepo anyamatawo anadza kwa ansembe aakulu ndi Afarisi; ndipo iwowa anati kwa iwo, Simunamtenge Iye bwanji?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

45 Pamenepo anyamatawo anadza kwa ansembe aakulu ndi Afarisi; ndipo iwowa anati kwa iwo, Simunamtenga Iye bwanji?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

45 Asilikali a ku Nyumba ya Mulungu aja adabwerera kwa akulu a ansembe ndi kwa Afarisi aja. Iwo adafunsa asilikaliwo kuti, “Bwanji simudabwere naye?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

45 Pomaliza asilikali a mʼNyumba ya Mulungu anabwerera kwa akulu a ansembe ndi Afarisi amene anawafunsa iwo kuti, “Kodi ndi chifukwa chiyani simunamugwire Iye?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 7:45
6 Mawu Ofanana  

Koma Petro anamtsata kutali, kufikira kubwalo la mkulu wa ansembe, nalowamo, nakhala pansi ndi anyamata, kuti aone chimaliziro.


Koma ena a mwa iwo anamuka kwa Afarisi, nawauza zimene Yesu adazichita.


Pamenepo ansembe aakulu ndi Afarisi anasonkhanitsa akulu, nanena, Titani ife? Chifukwa munthu uyu achita zizindikiro zambiri.


Afarisi anamva khamu la anthu ling'ung'udza zimenezi za Iye; ndipo ansembe aakulu ndi Afarisi anatuma anyamata kuti akamgwire Iye.


Izi ananena atate wake ndi amake, chifukwa anaopa Ayuda; pakuti Ayuda adapangana kale, kuti ngati munthu aliyense adzamvomereza Iye kuti ndiye Khristu, akhale woletsedwa m'sunagoge.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa