Yohane 7:42 - Buku Lopatulika42 Kodi sichinati chilembo kuti Khristu adza kutuluka mwa mbeu ya Davide, ndi kuchokera ku Betelehemu, kumudzi kumene kunali Davide? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Kodi sichinati chilembo kuti Khristu adza kutuluka mwa mbeu ya Davide, ndi kuchokera ku Betelehemu, kumudzi kumene kunali Davide? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Suja Malembo akuti kholo lake ndi mfumu Davide? Ndipo sujanso akuti adzachokera ku mudzi wa Betelehemu kumene Davideyo anali?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Kodi Malemba samanena kuti Khristu adzachokera mʼbanja la Davide, ndi ku Betelehemu mu mzinda umene Davide anakhalamo?” Onani mutuwo |