Yohane 7:41 - Buku Lopatulika41 Ena ananena, Uyu ndi Khristu. Koma ena ananena, Kodi Khristu adza kutuluka mu Galileya? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Ena ananena, Uyu ndi Khristu. Koma ena ananena, Kodi Khristu adza kutuluka m'Galileya? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Ena ankanena kuti, “Ameneyu ndiye Mpulumutsi wolonjezedwa uja.” Koma ena ankanena kuti, “Kodi Mpulumutsiyo nkuchokera ku Galileya ngati? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Ena anati, “Iye ndiye Khristu.” Komanso ena anafunsa kuti, “Kodi Khristu angachokere bwanji ku Galileya? Onani mutuwo |