Yohane 7:40 - Buku Lopatulika40 Pamenepo ena a khamulo pakumva mau awa, ananena, Mneneriyo ndi uyu ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Pamenepo ena a khamulo pakumva mau awa, ananena, Mneneriyo ndi uyu ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Pamene khamu la anthu lidamva mau ameneŵa, ena mwa iwo ankati, “Zoonadi munthuyu ndiye Mneneri uja.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Pakumva mawu ake, ena a anthuwo anati, “Zoonadi munthu uyu ndi mneneri.” Onani mutuwo |