Yohane 7:30 - Buku Lopatulika30 Pamenepo anafuna kumgwira Iye; koma palibe wina anamgwira kumanja, chifukwa nthawi yake siinafike. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Pamenepo anafuna kumgwira Iye; koma palibe wina anamgwira kumanja, chifukwa nthawi yake siinafike. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Pamenepo anthu adafuna kumgwira Yesu, koma panalibe ndi mmodzi yemwe amene adamkhudza, chifukwa nthaŵi yake inali isanafike. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Chifukwa cha izi iwo anayesa kumugwira Iye, koma palibe aliyense amene anayika dzanja lake pa Iye, chifukwa nthawi yake inali isanafike. Onani mutuwo |