Yohane 7:29 - Buku Lopatulika29 Ine ndimdziwa Iye; chifukwa ndili wochokera kwa Iye, nandituma Ine Iyeyu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ine ndimdziwa Iye; chifukwa ndili wochokera kwa Iye, nandituma Ine Iyeyu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Koma Ine ndikuŵadziŵa, chifukwa ndine wochokera kwa Iwo, ndipo ndiwo adandituma.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 koma Ine ndikumudziwa chifukwa ndichokera kwa Iyeyo ndipo ndiye amene anandituma Ine.” Onani mutuwo |