Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 7:25 - Buku Lopatulika

25 Pamenepo ena a iwo a ku Yerusalemu ananena, Kodi suyu amene afuna kumupha?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Pamenepo ena a iwo a ku Yerusalemu ananena, Kodi suyu amene afuna kumupha?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Pamenepo anthu ena a ku Yerusalemu adati, “Kodi munthu akufuna kumupha uja, si ameneyu?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Pa nthawi imeneyi anthu ena a ku Yerusalemu anayamba kufunsana kuti, “Kodi uyu si munthu uja akufuna kumuphayu?

Onani mutuwo Koperani




Yohane 7:25
3 Mawu Ofanana  

Musaweruze monga maonekedwe, koma weruzani chiweruziro cholungama.


Ndipo taona amalankhula poyera, ndipo sanena kanthu kwa Iye. Kapena kodi akulu adziwa ndithu kuti ndiye Khristu ameneyo?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa