Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 7:21 - Buku Lopatulika

21 Yesu anayankha nati kwa iwo, Ndinachita ntchito imodzi, ndipo muzizwa monse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Yesu anayankha nati kwa iwo, Ndinachita ntchito imodzi, ndipo muzizwa monse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Yesu adati, “Ndinangochita ntchito yozizwitsa imodzi yokha, nonsenu nkumadabwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Yesu anawawuza kuti, “Ine ndinachita chodabwitsa chimodzi ndipo inu mwadabwa.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 7:21
3 Mawu Ofanana  

Ndipo chifukwa cha ichi Ayuda analondalonda Yesu, popeza anachita izo tsiku la Sabata.


Ngati munthu alandira mdulidwe tsiku la Sabata, kuti chilamulo cha Mose chingapasulidwe; kodi mundikwiyira Ine, chifukwa ndamchiritsadi munthu tsiku la Sabata?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa