Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 7:20 - Buku Lopatulika

20 Khamu la anthu linayankha, Muli ndi chiwanda: afuna ndani kukuphani Inu?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Khamu la anthu linayankha, Muli ndi chiwanda: afuna ndani kukuphani Inu?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Koma khamu la anthu lidamuyankha kuti, “Wagwidwa ndi mizimu yoipa Iwe. Akufuna kukupha ndani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Gulu la anthu linayankha kuti, “Iwe ndiye wagwidwa ndi ziwanda. Ndani akufuna kukupha?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 7:20
11 Mawu Ofanana  

Kumkwanira wophunzira kuti akhale monga mphunzitsi wake, ndi kapolo monga mbuye. Ngati anamutcha mwini banja Belezebulu, sadzaposa kodi kuwatero apabanja ake?


Koma Afarisi pakumva, anati, Uyu samatulutsa ziwanda koma ndi mphamvu yake ya Belezebulu, mkulu wa ziwanda.


Koma Afarisi analinkunena, Atulutsa ziwanda ndi mphamvu zake za mfumu ya ziwanda.


pakuti adanena, Ali ndi mzimu wonyansa.


Koma ambiri mwa iwo ananena, Ali ndi chiwanda, nachita misala; mukumva Iye bwanji?


Ayuda anayankha nati kwa Iye, Kodi sitinenetsa kuti Inu ndinu Msamariya, ndipo muli ndi chiwanda?


Yesu anayankha, Ndilibe chiwanda Ine; koma ndilemekeza Atate wanga, ndipo inu mundipeputsa.


Ayuda anati kwa Iye, Tsopano tazindikira kuti muli ndi chiwanda. Abrahamu anamwalira, ndi aneneri; ndipo Inu munena, Munthu akasunga mau anga, sadzalawa imfa kunthawi yonse.


Koma pakudzikanira momwemo, Fesito anati ndi mau aakulu, Uli wamisala Paulo; kuwerengetsa kwako kwakuchititsa misala.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa