Yohane 7:20 - Buku Lopatulika20 Khamu la anthu linayankha, Muli ndi chiwanda: afuna ndani kukuphani Inu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Khamu la anthu linayankha, Muli ndi chiwanda: afuna ndani kukuphani Inu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Koma khamu la anthu lidamuyankha kuti, “Wagwidwa ndi mizimu yoipa Iwe. Akufuna kukupha ndani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Gulu la anthu linayankha kuti, “Iwe ndiye wagwidwa ndi ziwanda. Ndani akufuna kukupha?” Onani mutuwo |