Yohane 6:9 - Buku Lopatulika9 Pali mnyamata pano, amene ali nayo mikate isanu yabarele, ndi tinsomba tiwiri; koma nanga izi zikwanira bwanji ambiri otere? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pali mnyamata pano, amene ali nayo mikate isanu yabarele, ndi tinsomba tiwiri; koma nanga izi zifikira bwanji ambiri otere? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Pali mnyamata pano, ali ndi buledi msanu wabarele, ndi tinsomba tiŵiri. Koma zimenezi zingachitenji kwa anthu onseŵa?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Pano pali mnyamata amene ali ndi buledi musanu wabarele ndi tinsomba tiwiri, kodi zingakwane onsewa?” Onani mutuwo |