Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 6:8 - Buku Lopatulika

8 Mmodzi wa ophunzira ake, Andrea, mbale wake wa Simoni Petro, ananena ndi Iye,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Mmodzi wa ophunzira ake, Andrea, mbale wake wa Simoni Petro, ananena ndi Iye,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Wophunzira wake wina, dzina lake Andrea, mbale wake wa Simoni Petro, adauza Yesu kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Mmodzi wa ophunzira ake, Andreya, mʼbale wa Simoni Petro, anati,

Onani mutuwo Koperani




Yohane 6:8
3 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Yesu analikuyenda m'mbali mwa nyanja ya Galileya, anaona abale awiri, Simoni wonenedwa Petro, ndi Andrea, mbale wake, analikuponya khoka m'nyanja; popeza anali asodzi a nsomba.


Ndipo Yesu yemwe ndi ophunzira ake anaitanidwa kuukwatiwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa