Yohane 6:7 - Buku Lopatulika7 Filipo anayankha Iye, Mikate ya marupiya atheka mazana awiri siikwanira iwo, kuti yense atenge pang'ono. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Filipo anayankha Iye, Mikate ya marupiya atheka mazana awiri siikwanira iwo, kuti yense atenge pang'ono. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Filipo adayankha kuti, “Ngakhale ndalama mazana aŵiri sizingakwanire konse kugula chakudya choti aliyense mwa anthuŵa adyeko ngakhale pang'ono.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Filipo anamuyankha Iye kuti, “Malipiro a miyezi isanu ndi itatu sangathe kugula buledi okwanira aliyense kuti adye!” Onani mutuwo |