Yohane 6:6 - Buku Lopatulika6 Koma ananena ichi kuti amuyese; pakuti anadziwa yekha chimene adzachita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma ananena ichi kuti amuyese; pakuti anadziwa yekha chimene adzachita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 (Adaafunsa zimenezi dala kuti amuyese Filipoyo, koma mwiniwakeyo adaadziŵiratu choti achite.) Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iye anafunsa izi kumuyesa chabe, pakuti Iye ankadziwa chimene ankayenera kuchita. Onani mutuwo |