Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 6:10 - Buku Lopatulika

10 Nati Yesu, Akhalitseni anthu pansi. Ndipo panali udzu wambiri pamalopo. Pamenepo amunawo anakhala pansi, kuwerenga kwao monga zikwi zisanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Nati Yesu, Akhalitseni anthu pansi. Ndipo panali udzu wambiri pamalopo. Pamenepo amunawo anakhala pansi, kuwerenga kwao monga zikwi zisanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Yesu adati, “Auzeni anthu akhale pansi.” (Pamenepo panali msipu wambiri.) Anthuwo adakhaladi pansi. Amuna okha analipo ngati zikwi zisanu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Yesu anati, “Awuzeni anthuwa akhale pansi.” Pamalo pamenepa panali udzu wambiri ndipo amuna amene anakhala pansi anali osachepera 5,000.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 6:10
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anadyawo anali amuna monga zikwi zisanu, kuwaleka akazi ndi ana.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa